score
float32 1.04
1.25
⌀ | Chichewa
stringlengths 9
500
| Xhosa
stringlengths 9
500
⌀ |
---|---|---|
1.241936 |
Chinthu chilichonse chimene mudzapempha m'mapemphero anu, mudzalandira ngati muli ndi chikhulupiriro."
|
Kwaye nantoni na oyicelayo ngomthandazo, ukholwa, uya kuyifumana.
|
1.241869 |
Kodi kuuka kwa Yesu kunali kosiyana bwanji ndi kuuka kwa anthu ena m'mbuyomo?
|
Uvuko lukaYesu lwalahluke njani kuvuko lwabantu bangaphambi kwakhe?
|
1.241857 |
Koma anthu a mumzindawu anapitirizabe kuchita zoipa.
|
Sekunjalo, abantu beso sixeko baqhubeka nobubi babo.
|
1.241761 |
Ndipo cinatsegula pakamwa pace kukanena zamwano pa Mulungu, kucitira mwano dzina lace, ndi cihema cace, ndi iwo akukhala m'Mwamba.
|
Lawuvulela umlomo walo ekumnyeliseni uThixo, ukuba lilinyelise igama lakhe, nomnquba wakhe, nabo bahleli emazulwini.
|
1.241754 |
Iwo anauzidwa kuti: "Mitundu yonse ya anthu padziko lapansi adzaona kuti mukutchedwa ndi dzina la Yehova, ndipo adzachita nanu mantha."
|
Axelelwa oku: "Ziya kubona zonke izizwana zomhlaba ukuba igama likaYehova libizwe phezu kwakho, zikoyike."
|
1.241719 |
Mulungu amalonjeza anthu amene 'amaganizira za dzina lake' kuti: "Ndidzawachitira chifundo monga mmene munthu amachitira chifundo mwana wake amene amamutumikira."
|
UThixo uthembisa abo "bacinga ngegama lakhe" esithi: "Ndiza kubabonisa imfesane, kanye njengomntu obonisa imfesane kunyana wakhe omkhonzayo."
|
1.241701 |
Ukadzatuluka udzakhala wokalamba komanso wekhawekha."
|
Uya kuthi uphuma, ube ulixhegokazi elingenabani."
|
1.241693 |
18 Tonse tikhoza kutsatira mfundo ya m'mawu a Paulowa.
|
18 Sonke sinokufunda nto kula mazwi kaPawulos.
|
1.241671 |
Mawu Ake amatilimbikitsa 'kumufufuza ndi kumupeza, ngakhale sakhala patali ndi yense wa ife.'
|
ILizwi lakhe lisikhuthaza ukuba 'simphuthaphuthe size ngokwenene simfumane, nangona, enyanisweni, engekude kuye ngamnye wethu.'
|
1.241598 |
Popeza kuti saganiza bwino, zimawavuta kuti asiyanitse choyenera ndi chosayenera.
|
Xa amandla abo okucinga engasebenzi kakuhle, kuba nzima ukuba bahlule okulungeleyo kokubi.
|
1.241534 |
Ndipo iwo anapita kukamenyana ndi ana a Amoni.
|
Baphuma baya koonyana baka-Amon.
|
1.241532 |
"Wandipeza kodi mdani wanga?"
|
'Undifumene, lutshaba lwam!'
|
1.241502 |
Koma musaiwale kucitira cokoma ndi kugawira ena; pakuti nsembe zotere Mulunguakondweranazo.
|
ke ukwenza okuhle nobudlelane, musani ukukulibala; kuba imibingelelo enjalo uyakholiswa kakuhle yiyo uthixo.
|
1.241493 |
Kodi iweyo unayamba wanama? - * Ngakhale akuluakulu ena amene amakonda Mulungu ananamapo.
|
Ngaba wakha waxoka? - *Nkqu nabantu abadala abamthandayo uThixo bakha baxoka.
|
1.24149 |
Palibe tsiku kapena malire a kutsitsa,
|
Akukho mhla kwaye akukho mda umda ekukhupheleni,
|
1.241469 |
Zoyipa zonsezi zimatuluka mʼkati ndipo zimadetsa munthu."
|
Zonke ezi zinto zingendawo ziphuma ngaphakathi, zimenze inqambi umntu.
|
1.241465 |
Yesu anawawuza kuti, "Atate anga amagwira ntchito nthawi zonse mpaka lero lino, ndipo Inenso ndili pa ntchito."
|
Wawaphendula ke uYesu wathi, UBawo uyasebenza kude kube ngoku, nam ndiyasebenza.
|
1.24146 |
"Gula Choonadi Ndipo Usachigulitse"
|
"Thenga Inyaniso, Ungathengisi Ngayo"
|
1.241443 |
Ndipo mudziwa kuti Iyeyu anaonekera kudzachotsa machimo; ndipo mwa Iye mulibe tchimo.
|
Senazi ukuthi yena wabonakaliswa, ukuze asuse izono; akukho sono kuye.
|
1.241439 |
Pakuti ngakhale Khristu sanadzikondweretse yekha."
|
Kuba kwanoKristu akazange azikholise yena ngokwakhe."
|
1.241423 |
Kodi umadziŵa kuti nyenyezi zonse zili ndi mayina awo?
|
Ngaba ubusazi ukuba zonke iinkwenkwezi zinamagama?
|
1.241413 |
Iye anakopa Ayuda ambiri komanso anthu a mitundu ina.
|
Watsalela kuye inkitha yamaYuda neeNtlanga.
|
1.241374 |
Kodi kuuka kwa Yesu kunali kosiyana bwanji ndi kuuka kwa anthu ena m'mbuyomo?
|
Uvuko lukaYesu lwalahluke njani kolwabantu ababevuswe ngaphambi kwakhe?
|
1.241363 |
Thangwi yanji tisafunika kukumbuka nkazi wa Loti?
|
Kutheni sifanele sikhumbule umkaLote?
|
1.241328 |
6 Ifenso tikapirira tidzalandira mphoto.
|
6 Ukuba siyanyamezela, siya kufumana umvuzo.
|
1.241248 |
23 Atate wathu amafuna kuti tiyandikane naye.
|
23 UBawo wethu ufuna sisondele kuye.
|
1.24122 |
Rom 4:15 Pakuti chilamulo chichitira mkwiyo; koma pamene palibe lamulo pamenepo palibe kulakwa,
|
Ingqumbo kaThixo kaloku ibangwa kukwaphulwa komthetho wakhe; kodwa apho ungekhoyo umthetho akukho kwaphulwa kwamthetho.
|
1.241198 |
Baibulo limati: "Awiri aposa mmodzi; pakuti ali ndi mphotho yabwino m'ntchito zawo.
|
"Ababini balunge ngakumbi kunomnye, ngenxa yokuba banomvuzo ngomsebenzi wabo onzima.
|
1.241196 |
Nʼchifukwa chiyani ena a inu mukuganiza kuti nʼkosatheka kuti Mulungu aukitse akufa?
|
Yini na ukuba nithi, yinto eningenakukholwa yiyo, ukuba uThixo uyabavusa abafileyo?
|
1.241065 |
Kodi Mulungu amafuna kuti tizikondwerera masiku amene tinabadwa? -
|
Ngaba uThixo ufuna sibhiyozele imihla yokuzalwa? -
|
1.241014 |
'Ndodo yake yachifumu ndi ndodo yachilungamo' choncho n'zosachita kufunsa kuti iye ndi wolamulira wachilungamo komanso wosakondera.
|
'Intonga yobukhosi yobukumkani bakhe yintonga yobukhosi yokuthe tye,' ukuqinisekisa ukuba ulawula ngobulungisa yaye akakhethi buso.
|
1.241 |
Koma kodi mukudziwa kuti timaphunziranso Baibulo ndi anthu padziko lonse?
|
Kodwa ubusazi na ukuba sikwafundisa abantu iBhayibhile emhlabeni wonke?
|
1.240959 |
Kuopa Mulungu ndiko maziko a nzeru zenizeni.
|
Ukoyika uThixo kusisiseko sobulumko bokwenyaniso.
|
1.240957 |
Cotero munthu ali yense wa ife adzadziwerengera mlandu wace kwa Mulungu.
|
Ngoko ke elowo kuthi uya kuziphendulela kuThixo.
|
1.240957 |
Cotero munthu ali yense wa ife adzadziwerengera mlandu wace kwa Mulungu.
|
ngoko ke elowo kuthi uya kuziphendulela kuthixo.
|
1.240931 |
Iye ndi bwenzi loposa onse.
|
Ngoyena mhlobo ulungileyo.
|
1.240928 |
Ndipo mkaziyo unamuona, ndiye mudzi waukuru, wakucita ufumu pa mafumu a dziko.
|
Inkazana owayibonayo nguloo mzi mkhulu, ulawula ookumkani bomhlaba.
|
1.240903 |
Kodi ndikhoza kukhumudwitsa ena?'
|
Ngaba andiyi kubakhubekisa abanye?'
|
1.240828 |
30Ndipo mumati, 'Ngati tikanakhala mʼmasiku a makolo athu sitikanakhetsa nawo magazi a aneneri.' 31Potero mukutsimikiza kuti muli ana a iwo amene anapha aneneri.
|
Nithi: 'Ukuba sasikho thina kwimihla yoobawo, ngesingahambisananga nabo ngokubulawa kwabashumayeli.'
|
1.240798 |
Iye anati: "Sindine woposa makolo anga."
|
Wathi: "Andilunganga ngaphezu kookhokho bam."
|
1.240794 |
17 Ananso ayenera kukhala odekha.
|
17 Nabo abantwana kufuneka bazole.
|
1.240761 |
iwo anaona ophunzira ake akudya chakudya ndi mʼmanja mwakuda kapena kuti mʼmanja mosasamba.
|
bathi, bakubona abathile kubafundi bakhe besidla isonka ngezandla eziziinqambi, oko kukuthi ngezingahlanjwanga, basuka basola.
|
1.240678 |
Munthu amene akuyenda alibe ulamuliro wowongolera mapazi ake."
|
Asikokomntu ohambayo ukwalathisa inyathelo lakhe."
|
1.240653 |
Tikukupatsani mafungulo onse.
|
Sikunika zonke izitshixo.
|
1.240613 |
Ndingakonde kukusonyeza dzinali m'Baibulo."
|
Ndithand' ukukubonis' eBhayibhileni."
|
1.240564 |
20 Kodi tingakhale tani na cikhulupiro ninga ca Djobi?
|
20 Singaba nalo njani ukholo olufana nolukaYobhi?
|
1.240528 |
Kunena zoona, adani a munthu adzakhala a m'banja lake lenileni."
|
Eneneni, iintshaba zomntu ziya kuba ngabantu bendlu yakhe."
|
1.240471 |
Koma iye amene anali wa mkazi waufulu anabadwa mwa lonjezo.
|
Ke yena lowo womfazi okhululekileyo wayezelwe ngalo idinga.
|
1.240408 |
Tsiku limenelo atumwiwo ananena kuti: "N'zoonadi, Ambuye wauka kwa akufa ndipo waonekera kwa Simoni!"
|
Abapostile bathi ngaloo mini: "Enyanisweni iNkosi ivusiwe yaye ibonakele kuSimon!"
|
1.2404 |
Kodi bambo adakali moyo?'
|
Utata usaphila kodwa?'
|
1.240397 |
12 N'kutheka kuti izi n'zimene zinachitikira Akhristu ena a ku Tesalonika.
|
12 Kusenokuba kwenzeka ezo zinto kanye kwabathile baseTesalonika.
|
1.240382 |
Ndiye Yosefe anawakhululukira.
|
Ngoko uYosefu wabaxolela.
|
1.240329 |
ndi kukhala naco cikhulupiriro ndi cikumbu mtima cokoma, cimene ena adacikankha, cikhulupiriro cao cidatayika;
|
unokholo nesazela esilungileyo, ethe inxenye, isigibile, yaphukelwa ngumkhombe mayelana nokholo;
|
1.240283 |
Koma Mulungu amafuna kuti amene amamulambira azikhulupirira kuti iye alikodi komanso kuti amawakonda.
|
Kodwa yena ke uThixo ufuna abo bamkhonzayo baqiniseke ukuba ukho yaye uyabathanda.
|
1.24027 |
Ndinalibe ndalama zoyendera kupita ku New York.
|
Ndandingenamali yokuya eNew York.
|
1.240177 |
Ulamuliro wake ndiye ulamuliro wamuyaya woti sudzatha, ndi ufumu wake sudzaonongeka. ."
|
Ulawulo lwakhe lulawulo oluhlala ngokungenammiselo olungayi kudlula, nobukumkani bakhe bobungayi konakaliswa."
|
1.240082 |
(Juwau 8:44) Iye adakhala nyamagunkha ndipo adapandukira Mulungu.
|
(Yohane 8:44) Waba lixoki elavukela uThixo.
|
1.240032 |
Munthu akagwiritsitsa nzeru, zidzakhala ngati mtengo wa moyo kwa iye, ndipo ozigwiritsitsa adzatchedwa odala."
|
Bungumthi wobomi kwabo babubambayo, nabo babubamba nkqi kuya kuthiwa banoyolo."
|
1.240017 |
Anapulumutsidwa "Pamodzi ndi Anthu Ena 7"
|
Wasindiswa "Nabanye Abasixhenxe"
|
1.240011 |
Kodi kalata ya Yohane ingatithandize bwanji pa nkhaniyi?
|
Incwadi kaYohane inokusinceda njani senze loo nto?
|
1.239959 |
chifukwa aliyense amene anafa anamasuka ku tchimo.
|
ngokuba ofileyo ukhululiwe esonweni.
|
1.239896 |
Kodi sindine mtumwi?
|
Andinguye na andimpostile?
|
1.239886 |
Mʼmalo mwake tsono, muyenera kumukhululukira ndi kumulimbikitsa mtima kuti asamve chisoni choposa muyeso, angataye mtima.
|
ngokokude nithi kanye senimxolela, nimthuthuzele, hleze lowo unjalo aselesuka edliwa kukuba buhlungu ngokugqithiseleyo.
|
1.239873 |
Olalikira ndi zolinga zabwinowa amachita izi mwachikondi, podziwa kuti ine ndili muno chifukwa cha kuteteza Uthenga Wabwino.
|
Abo ke baqhutywa luthando, kuba bayazi ukuba uThixo undiphathise umsebenzi wokukhusela udaba olungoKrestu.
|
1.239873 |
ndipo sanamdziwe iye kufikira atabala mwana wake; namutcha dzina lake Yesu.
|
waza ke akamazi, wada wazala unyana wakhe wamazibulo; wambiza ke ngegama elinguYesu.
|
1.239822 |
Ndipo pamene mupemphera musabwebwe zambiri, monga akunja; chifukwa akuganiza kuti adzamveka ngati alankhula mawu ambiri.
|
Ke xa nithandazayo ze ningenzi milembelele ingento njengabangakholwayo, bona baba boviwa ngenxa yamazwi abo amaninzi.
|
1.239818 |
amene makolo athu sanafuna kumvera iye, koma anamkankha acoke, nabwerera m'mbuyo mumtima mwao ku Aigupto,
|
abangathandanga kumlulamela oobawo bethu, besuka bamgiba, babuyela eYiputa ngeentliziyo zabo,
|
1.239816 |
Kenako anauza Yosefe kuti: "Popeza kuti Mulungu wakudziwitsa zonsezi, palibenso munthu wina wozindikira ndi wanzeru ngati iwe.
|
KuYosefu wathi: "Ekubeni uThixo ekwazisile konke oku, akukho bani uyingqondi nosisilumko njengawe.
|
1.239812 |
Iwo ankachita zonse zimene angathe kuti andifike pamtima.
|
Bazama yonke into ukuze bafikelele intliziyo yam.
|
1.239803 |
"Musamakhulupirire anthu olemekezeka, kapena mwana wa munthu wina aliyense wochokera kufumbi amene alibe chipulumutso.
|
"Musani ukukholosa ngamanene, ngonyana womntu, yena ungenalo usindiso.
|
1.239771 |
Anthu amene ali m'gulu la kapolo wokhulupirikayu adzapatsidwa udindowu pamene adzalandira mphoto yawo yolamulira limodzi ndi Khristu kumwamba.
|
Abo babumba eli khoboka lithembekileyo baya kumiselwa xa befumana umvuzo wokuphila ezulwini, balawule kunye noKristu.
|
1.239761 |
Popeza Mulungu ndi wamuyaya, zaka 1,000 zili ngati tsiku limodzi kwa iye.
|
Ekubeni enguThixo kanaphakade, iminyaka eliwaka kuye ifana nosuku.
|
1.239761 |
"Iye Sali Kutali ndi Aliyense wa Ife"
|
'Akakho kude kuye ngamnye wethu.'
|
1.239742 |
Ndipo ananena kwa ine, Tapenya, usachite; ndine kapolo mnzako, ndi mnzao wa abale ako aneneri, ndi wa iwo akusunga mau a buku ili; lambira Mulungu.
|
Sithi kum, Lumka, ungenjenjalo; kuba ndingumkhonzi kunye nawe, nabazalwana bakho abaprofeti, nabo bawagcinayo amazwi ale ncwadi; qubuda kuThixo.
|
1.239739 |
Muzifunafuna Ufumu Osati Zinthu Zina
|
Funa UBukumkani, Kungekhona Izinto
|
1.239732 |
Pakuti iye analamula ndipo zinalengedwa.+
|
Kuba yena wayalela, zona zadalwa.+
|
1.239707 |
amene makolo athu sanafuna kumvera iye, koma anamkankha achoke, nabwerera m'mbuyo mumtima mwao ku Ejipito,
|
abangathandanga kumlulamela oobawo bethu, besuka bamgiba, babuyela eYiputa ngeentliziyo zabo,
|
1.239704 |
Nthaŵi zonse Mulungu wathu sadzataya amene ali okhulupirika kwa iye.
|
UThixo wethu akasayi kuze nanini na abashiye abo banyanisekileyo kuye.
|
1.239698 |
Pakuti chilengedwe chikudikira ndi chiyembekezo kuonetsedwa poyera kwa ana a Mulungu.
|
Kuba indalo ilinde ngolangazelelo olukhulu ukutyhilwa koonyana bakaThixo.
|
1.239691 |
Kodi mutha kupulumuka sabata yatha?
|
Ngaba ungasinda kwiveki ephelileyo?
|
1.239664 |
Ndiye dzifunseni kuti, 'Kodi n'kutheka kuti Mulungu akugwiritsa ntchito anthu amenewa pofuna kundikokera kwa iye?'
|
Khawuzibuze, 'Ngaba mhlawumbi uThixo usebenzisa wona ukuze afike nakum?'
|
1.239633 |
Tsono pomwe idafika nthawe ya bzisapo, iye adatumiza kapolo wace kwa alimiwo kuti akatambire bzisapo bzinango bza m'munda wa mpesayo.
|
Ngexesha lokuvuthwa kweziqhamo ke, wathumela isicaka kubaqeshi, ukuze bamnike imali yengqesho.
|
1.239624 |
Kodi n'cifunilo ca Mulungu kuti ife anthu tizifa?
|
Ngaba ukufa kukuthanda kukaThixo ngoluntu?
|
1.239605 |
Mose sanathe kuona Mulungu, koma anamva mawu a Mulungu.
|
UMoses wayengenakumbona uThixo, kodwa waliva ilizwi likaThixo.
|
1.239596 |
Nikodemo ananena kwa Iye, Munthu akhoza bwanji kubadwa atakalamba?
|
Uthi uNikodemo kuye, Angathini na umntu ukuzalwa emdala?
|
1.239578 |
Koma ndikuwuzani kuti musalumbire ndi pangʼono pomwe kutchula kumwamba chifukwa kuli mpando waufumu wa Mulungu.
|
Ke mna ndithi kuni, Maningakhe nifunge nto; nokuba lizulu,ngokuba yitrone kaThixo;
|
1.239568 |
Pakuti ayenera kuchita ufumu kufikira [Mulungu] ataika adani onse pansi pa mapazi ake.
|
Kuba umelwe yena kukuthi alawule, ade azibeke phantsi kweenyawo zakhe zonke iintshaba.
|
1.239542 |
"Palibenso Thanthwe Longa Mulungu Wathu"
|
"Akukho Liwa LinjengoThixo Wethu"
|
1.23953 |
Mbwenye Salomoni amanga banja na akazi azinji a madziko anango, akuti akhalambira madzimunthu.
|
Kodwa uSolomon watshata abafazi abaninzi ababehlala kwamanye amazwe, ibe aba bafazi babenqula izithixo.
|
1.239517 |
Koma ayamikidwe Mulungu, kuti ngakhale mudakhala akapolo a uchimo, tsopano mwamvera ndi mtima makhalidwe aja a chiphunzitso chimene munaperekedweracho;
|
Ke kaloku, makubulelwe kuThixo, kuba nanifudula nilawulwa sisono, kodwa ngoku niyithobela ngokupheleleyo imfundiso eniyifundisiweyo.
|
1.239504 |
Kodi Yesu ankatanthauza chiyani pamene anati: "Iwe udzakhala nane m'Paradaiso"?
|
Wayethetha ukuthini uYesu xa wathi: "Uya kuba nam eParadesi"?
|
1.239502 |
Matauni 5 ku France komwe mungakonde kukhala
|
Iidolophu ezi-5 eFrance apho ungathanda ukuhlala khona
|
1.239477 |
Ndipo pamene mupemphera musabwebwe zambiri, monga akunja; chifukwa akuganiza kuti adzamveka ngati alankhula mawu ambiri.
|
Nithandaza njalo ke, maningenzi milembelele ingeyanto,njengabeentlanga; kuba beba boviwa ngenxa yamazwi abo amaninzi.
|
1.239455 |
Koma pamenepo ine ndidzawauza mwachimvekere kuti: Sindinakudziweni konse chiyambire!
|
Ukanti ndiya kwandula ndivume kubo ndithi: Andizange ndinazi!
|
1.239448 |
Ine ndi Atate ndife amodzi.
|
Mna noBawo simnye. "
|
1.239447 |
Anthu osaona ndi olumala anabwera kwa Iye mʼNyumba ya Mulungu ndipo anawachiritsa.
|
Kweza kuye iimfama neziqhwala, etempileni apho, waziphilisa.
|
1.239427 |
Koma tsono musakondwere kwambiri kuti mizimu inakugonjerani, koma kuti mukondwere ngati mayina anu alembedwa m'mwamba.
|
Noko ke maningakuvuyeli oku, kokuba oomoya benithobele; vuyelani ke kanye okokuba amagama enu ebhaliwe emazulwini.
|
1.239396 |
Ndipo iwo anaponyera fumbi pamitu pawo, nafuwula, akulira, ndi kulira, nanena, Tsoka, tsoka, mudzi waukulu, m'mene onse okhala nazo zombo m'nyanja analemera ndi cuma cace; pakuti iye anawonongedwa mu ora limodzi.
|
Bagalela uthuli entloko, Bamana bedanduluka, belila,besenza isijwili, Besithi, Yeha, yeha, mzimkhulu, Apho baba nobutyebi khona bonke aba baneenqanawa elwandle, ngeento ezinqabileyo zawo!
|
1.239266 |
Abale athu amatisamalira bwino tsiku ndi tsiku.
|
Abazalwana basinyamekela yonke imihla.
|
1.239226 |
Kenako iye sanaonekenso, chifukwa Mulungu anam'tenga."
|
Wandula ke wanyamalala, kuba uThixo wamthabatha."
|
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.