score
float32 1.04
1.25
⌀ | Chichewa
stringlengths 9
500
| Xhosa
stringlengths 9
500
⌀ |
---|---|---|
1.244532 |
Pamenepo ophunzirawo anati: 'Ambuye, ngati iye akupumula, apeza bwino.'
|
Ngoko ke abafundi bathi kuye: 'Nkosi, ukuba uye kuphumla, uya kuphila.'
|
1.24446 |
1Co 6:8 Koma muyipsa, nimunyenga, ndipo mutero nawo abale anu.
|
6:8 Ke nina nenza ukuzenzakalisa kunye ukukopela, yaye oku kubo abazalwana!
|
1.244442 |
Nthawi zina ndinkamva ngati mneneri Danieli, yemwe atalandira mawu aulosi kuchokera kwa mngelo ananena kuti: "Ndinamva zimene ananenazo, koma sindinadziwe tanthauzo lake."
|
Ndandifana nomprofeti uDaniyeli, owathi emva kokufumana isiprofeto kwingelosi: "Ndakuva oko, kodwa andakuqonda."
|
1.244438 |
Dziko lonse silili pamaso pako kodi?
|
Aliphambi kwakho na ilizwe lonke?
|
1.244436 |
N'chifukwa chiyani Mose ankaona kuti utumiki wake ndi wofunika kwambiri?
|
Kwakutheni ukuze uMoses asixabise isabelo sakhe?
|
1.244415 |
Koma n'zomvetsa chisoni kuti mkazi wanga wokondedwa, Maria, anamwalira mu 2014.
|
Ngelishwa, inkosikazi yam endiyithanda kunene, uMaria, yasweleka ngo-2014.
|
1.244402 |
ndipo sindidzakumbukiranso machimo awo."
|
kwaye abayi kuphinda bakhumbule izono zabo.
|
1.244398 |
Ndipo pamene adakhuta, Iyeananena kwa akuphunzira ace, Sonkhanitsani makombo kuti kasatayike kanthu.
|
Bakuhlutha ke, uthi kubafundi bakhe, Buthani amaqhekeza aseleyo, ukuze kungonakali nto.
|
1.244375 |
44 Koma iwo adaganiza kuti Iye adali m'chipilingu cha ulendo, nayenda ulendo wa tsiku limodzi; ndipo adayamba kumfunafuna Iye mwa abale awo ndi mwa anansi awo.
|
44 Babeba ke bona usemkhokweni wabahambi, bahamba uhambo lwamini-nye; bamana bemfuna phakathi kwemizalwana, naphakathi kwabazana nabo.
|
1.244375 |
Pakuti mau a mtanda ali ndithu cinthu copusa kwa iwo akutayika, koma kwa ife amene tirikupulumutsidwa ali mphamvu ya Mulungu.
|
Kuba ilizwi lomnqamlezo libubudenge okunene kwabatshabalalayo; kodwa ke kwabasindiswayo, thina aba, lingamandla kaThixo.
|
1.244374 |
Mulungu sanalenge anthu kuti azifa, koma kuti azikhala ndi moyo wosatha.
|
UThixo akazange abadalele ukuba bafe abantu kodwa wayefuna baphile ngonaphakade.
|
1.244287 |
kapena ngati munthu waganyu woyembekezera malipiro ake,
|
Okanye anike uThixo intlawulelo ngaye;
|
1.244282 |
Tsiku lililonse, mlongo wanga anabwera.
|
Yonke imihla, kweza udade wam.
|
1.244254 |
Kodi tiyenera kuopa Mulungu chifukwa choti ndi wamphamvu?
|
Ngaba sifanele simoyike uThixo ngenxa yokuba enamandla?
|
1.244208 |
Nanga kodi pali nthawi zina pamene amawachitira chifundo?'
|
Ngaba kukhe kuthethe izenzo zenceba?'
|
1.244207 |
Unakhulupirika pa zinthu zochepa.
|
Ubuthembekile kwizinto ezimbalwa.
|
1.244185 |
Tsopano muyenera kumukhululukira ndi kumtonthoza, kuti asataye mtima ndi chisoni chochuluka.
|
ngokokude nithi kanye senimxolela, nimthuthuzele, hleze lowo unjalo aselesuka edliwa kukuba buhlungu ngokugqithiseleyo.
|
1.244131 |
Kodi kupha nyama n'kulakwa?
|
Ngaba kuphosakele ukubulala izilwanyana?
|
1.244127 |
Akulu awiri anapita kukamuona.
|
Abadala ababini bamtyelela.
|
1.244082 |
Baibulo limanena kuti: "Kudzakhala kuuka kwa olungama ndi osalungama."
|
IBhayibhile ithi: "Kuza kubakho uvuko lwamalungisa nabangengomalungisa."
|
1.244062 |
Iye alonga pontho: 'Mbwenye cincino ndisadziwa kuti Mulungu anadzakupasani pyonsene pinamphemba imwe.'
|
Kodwa nangoku ndiyazi ukuba uThixo wokunika nantoni na oyicelayo kuye. ""
|
1.244041 |
Choncho musalole kuti Satana akupusitseni.
|
Ngoko ungaqhathwa nguSathana.
|
1.243992 |
39Koma ife sindife amodzi a iwo obwerera mʼmbuyo mwa mantha ndi owonongedwa, koma ndife amodzi a amene akukhulupirira ndi wopulumutsidwa.
|
Ke thina asingabahlehla baye entshabalalweni; singabokholo olusa ekuzuzeni umphefumlo.
|
1.243959 |
Nanga kodi n'zotheka kudzakhaladi m'Paradaiso?'
|
Ngaba ingaze ibekho nyhani?'
|
1.243937 |
Ndani tsopano adzakhala ndi zinthu zonse zimene unazisunga?'
|
Ngobu busuku uzakufa, Ziyakuba zezikabani ezi zinto uziqokekeleyo?
|
1.243896 |
Zomwe anthu adachitazi adayamba kuseka, chifukwa adadziwa kuti mtsikanayo wamwalira.
|
Kodwa bamwa ngentsini behlekisa ngaye uYesu, kuba besazi ukuba umntwana ufile.
|
1.243855 |
Iye ndi Atate wachikondi ndipo ankateteza komanso kusamalira atumiki ake okhulupirika monga Nowa, Abulahamu ndiponso Davide.
|
Ekubeni enguBawo onothando, ebebakhusela yaye ebanyamekela abakhonzi bakhe abanyanisekileyo abafana noNowa, uAbraham noDavide.
|
1.243813 |
Choncho iye anamuitanitsa ndi kumuuza kuti, 'Kodi ndikumva za iwe?
|
Ngoko wabizela kuye waza wathi kuye, 'Yintoni na le ndiyivayo ngawe?
|
1.243776 |
Onse ankadziwa kuti ayenera kupemphera kwa ndani.
|
Babesazi ukuba kufanelwe kuthandazwe kubani.
|
1.243726 |
amene musungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mwa chikhulupiriro, kufikira chipulumutso chokonzeka kukavumbulutsidwa nthawi yotsiriza.
|
nina bathe ngamandla kaThixo ngokholo balondolozelwa elusindisweni, olulungiselwe ukutyhilwa ngexesha lokugqibela.
|
1.243719 |
Iye sanali ngati David, kapena inu, kapena ine.
|
Waye akaba njengoDavide, okanye, okanye mna.
|
1.243667 |
Dzichepetseni pamaso pa Ambuye, ndipo Iye adzakukwezani.
|
Zithobeni phambi kweNkosi, njalo izaliphakamisa.
|
1.243649 |
Ndipo adapereka ena akhale atumwi, ena ngati aneneri, ena ngati alaliki, ena ngati abusa ndi aphunzitsi, " (Aefeso 4: 11)
|
Waza kwayena wabapha abanye ukuba babe ngabapostile, abanye babe ngabaprofeti, abanye babe ngabashumayeli beendaba ezilungileyo, abanye babe ngabalusi nabafundisi,
|
1.243647 |
Yezu atsandzaya pidabva iye mphangwa zenezi, mbalonga: 'Ndikuona Sathani agwa kale ninga njazi buluka kudzulu.
|
Wathi ke kubo: "Ndibone uSathana esiwa ezulwini okombane.
|
1.243486 |
pakuti Mzimu Woyera adzaphunzitsa inu nthawi yomweyo zimene muyenera kuzinena.
|
kuba uMoya oyiNgcwele uya kuthi ngelo xesha anifundise oko manikuthethe."
|
1.243472 |
Kampani yathu ali oposa 20 inde ...
|
Inkampani yethu ngaphezu kwama-20 ewe ...
|
1.243447 |
Dziko lapansili silidzawonongedwa ndi moto kapena china chilichonse.
|
Umhlaba awuzukutshatyalaliswa ngomlilo okanye ngenye indlela.
|
1.243402 |
Ndipo dziko silinathe kuwakwanira iwo, kuti akhale pamodzi: chifukwa kuti chuma chawo chinali chambiri, ndipo sanathe kukhala pamodzi.
|
Ilizwe elo alaba nakubathwala, ukuba bahlale ndawonye; ngokuba impahla yabo yayininzi, ababa nakuhlala ndawonye.
|
1.243394 |
"Kenako [Yesu Khristu] anagwira chinjoka, njoka yakale ija, amene ndi Mdyerekezi ndiponso Satana, ndi kumumanga zaka 1,000.
|
'Wayibamba uYesu Kristu inamba, loo nyoka yantlandlolo, enguMtyholi, uSathana, waza wayibopha iminyaka eliwaka.
|
1.243366 |
Lonjezoli liyenera kuti linalimbikitsa Zekariya.
|
UZekariya umele ukuba womelezwa sesi sithembiso.
|
1.243345 |
KODI zinthu zinali bwanji zaka masauzande apitawo?
|
KWAKUPHILWA njani kumawaka eminyaka eyadlulayo?
|
1.243327 |
Sizikutanthauza kuti Mulungu ankayendadi ndi Nowa padziko lapansili kapena Nowa anapita kumwamba n'kumakayenda ndi Mulungu.
|
Yayingathethi kuthi uThixo wayehamba emhlabeni okanye uNowa yena waya ezulwini.
|
1.243218 |
Mulungu ali ndi malo enieni amene amakhala ndipo ndi kumwamba.
|
UThixo unendawo ahlala kuyo - isezulwini.
|
1.24319 |
Iye anati: "Pamene ine ndi mkazi wanga tinkada nkhawa kwambiri, tinkapempha wachibale wina, yemwe ndi mkulu mu mpingo, kuti abwere kudzapemphera nafe.
|
Uthi: "Sinomkam sasisithi xa kunzima sicele isalamane sethu esingumdala webandla ukuba size kuthandaza nathi.
|
1.243166 |
20 - Milandu imene tawina ku Khoti Loona za Ufulu wa Anthu ku Ulaya kuyambira mu April 2000
|
20 - Amatyala esiye saphumelela kuwo kwiEuropean Court of Human Rights ukususela ngoAprili 2000
|
1.243152 |
Koma Nyumba ya Mulungu imene amanena linali thupi lake.
|
Yena ke wayethetha ngetempile yomzimba wakhe.
|
1.243147 |
Anakukonzera zimenezi pa tsiku limene unalengedwa.
|
Zalungiswa ngemini owadalwa ngayo.
|
1.243115 |
Zoipa za tsiku lililonse n'zokwanira pa tsikulo.'
|
Imini nganye inobayo ububi obuyilingeneyo."
|
1.243091 |
Big tech: 'tikufuna thandizo lanu'
|
Itekhnoloji enkulu: 'sifuna uncedo lwakho'
|
1.24309 |
Farao akuuza Yosefe maloto ake: 'Ndinaona ng'ombe zisanu ndi ziwiri zonenepa, zokongola.
|
UFaro uxelela uYosefu amaphupha akhe: 'Ndibone iimazi zeenkomo ezisixhenxe ezityebileyo, ezintle.
|
1.243066 |
Ndipo pomwepo ambiri adzakhumudwa, nadzaperekana wina ndi mzache.
|
Ngelo xesha baninzi abaya kukhutyekiswa, banikelane, bathiyane.
|
1.243041 |
"Palibe Thanthwe Lofanana Ndi Mulungu Wathu"
|
"Akukho Liwa LinjengoThixo Wethu"
|
1.242983 |
Nthaŵi zonse Mulungu wathu sadzataya anthu amene ali okhulupirika kwa iye.
|
UThixo wethu akasayi kuze nanini na abashiye abo banyanisekileyo kuye.
|
1.242937 |
NI NTHAWI ya msonkhano wofunika kwambili m'Yerusalemu.
|
LIXESHA lentlanganiso ebaluleke kakhulu eYerusalem.
|
1.242937 |
Farao ndi antchito ake onse anaona kuti Yosefe wanena zanzeru.
|
UFaro nabanye abasebenzi bakhe balibona lilelobulumko icebo likaYosefu.
|
1.242895 |
Kulambira Koona Kumagwirizanitsa Anthu
|
Unqulo lokwenyaniso lumanyanisa abantu
|
1.242878 |
Koma ife tinamuyankha kuti, "Si nkhosa zanu, ndi nkhosa za Mulungu."
|
Saphendula sathi, "Ayizozakho, zezikaThixo."
|
1.242877 |
Pa tsiku limeneli, Mulungu adzawononga anthu onse oipa.
|
Ngelo xesha, uThixo uza kubasusa bonke abantu abangendawo.
|
1.242875 |
Pakuti iye adzakhala wamkulu pamaso pa Ambuye, ndipo sadzamwa konse vinyo kapena kachasu; nadzadzazidwa ndi Mzimu Woyera, kuyambira asanabadwe.
|
Kuba uya kuba mkhulu emehlweni eNkosi, angakhe asele wayini nasiselo sinxilisayo; uya kuzaliswa nguMoya oyiNgcwele kwasekuzalweni kwakhe.
|
1.242858 |
Ndi chikhulupiriro chimenechi makolo athu akale anayamikidwa.
|
Kuba amanyange angqinelwa ngokuba nalo olo.
|
1.242814 |
"Tiuzeni, Kodi Zinthu Zimenezi Zidzachitika Liti?"
|
"Sixelele, Ziya Kubakho Nini Na Ezi Zinto?"
|
1.24281 |
Mfumu yanzeru Solomo inalemba kuti: "Kanthu kali konse kali ndi nthawi yake."
|
UKumkani uSolomon owayesisilumko wathi: "Yonke into inexesha layo elimisiweyo."
|
1.242805 |
Iwo ayenera kuti anaphunzitsa mwana wawo, dzina lake Samisoni, chilamulo cha Mulungu ndipo zotsatira zake zinali zabwino.
|
Ngokuqinisekileyo bafundisa unyana wabo, uSamson, umthetho kaThixo yaye imigudu yabo yaphumelela.
|
1.242784 |
42Mfumu yayikazi yakummwera idzayimirira pa tsiku lachiweruzo ndi mʼbado uwu ndipo idzawutsutsa pakuti inachokera kumathero a dziko lapansi kudzamva nzeru za Solomoni, ndipo pano pali woposa Solomoni.
|
Ukumkanikazi welasezantsi uya kusuka eme ngomgwebo nesi sizukulwana, asigwebe; ngokuba wavela eziphelweni zomhlaba, esiza kuva ubulumko bukaSolomon; kanti ke omkhulu kunoSolomon nanku apha.
|
1.242722 |
amene anakhala wokhulupirika kwa iye adamuikayo, monganso Mose m'nyumba yace yonse.
|
Wathembeka kiloyo owamkhethako wambeka njengoMosi owabegade anjalo kiyo yoke indlu kaZimu.
|
1.24268 |
Ndatero kuti mudziwe ndithu kuti mawu amene munaphunzitsidwa ngoonadi.
|
ukuze uyazi kakuhle ingqiniseko yamazwi owafundisiweyo ngomlomo.
|
1.242669 |
Popeza wadzichepetsa chifukwa cha ine, sindidzabweretsa tsokali m'masiku ake.
|
Ngenxa yokuba ezithobile ngenxa yam, andiyi kuyizisa intlekele ngemihla yakhe.
|
1.242649 |
Pali chimene chachitika kapena?'" - Masami, Japan.
|
Ngaba kukho into eyenzekileyo?'" - uMasami waseJapan.
|
1.242642 |
Watsegula bwanji maso ako?"
|
Uwavule njani na amehlo akho?"
|
1.242561 |
"Koma khalani akuchita mawu, osati akumva okha, ndi kudzinyenga nokha ndi mabodza.
|
"Yibani ngabenzi belizwi hayi ngumphulaphuli kuphela, belahlekisa ngokwenu.
|
1.242494 |
Iye anayankha kuti, "Ndinaona Satana akugwa kuchokera kumwamba ngati mphenzi.
|
Wathi ke kubo: "Ndibone uSathana esiwa ezulwini okombane.
|
1.242454 |
Tiyeni tisankhe m'tsogoleri watsopano m'malo mwa Mose, ndi kubwerera ku Igupto!'
|
Masizinyulele inkokeli entsha endaweni kaMoses, size sibuyele eYiputa!'
|
1.242413 |
Iwo anati, "Munthu uyu akukopa anthu kuti azipembedza Mulungu mwanjira zotsutsana ndi malamulo athu."
|
esithi, Lo uzamela ukweyisa abantu ukuba bamhlonele uThixo ngokunxamnye nomthetho.
|
1.242398 |
Kodi mungathandize bwanji anthu odwala komanso okalamba?
|
Ungabasiza njani abantu abagulako nabalupheleko?
|
1.24237 |
Zimenezi sizinkandisangalatsa kwenikweni." - James. *
|
Zange ihle kamnandi kum le nto!" - UJames. *
|
1.242331 |
Mwamuna amene akufuna kukwatira ayenera kukonzekera bwino udindo umenewo.
|
Indoda efuna ukutshata ifanele iyilungele le mbopheleleko.
|
1.242291 |
Koma aliyense amene ataya moyo wake, chifukwa cha Ine, ndi chifukwa cha Uthenga Wabwino, adzaupulumutsa.
|
Osukuba ke eya balahlekelwe ubomi bakhe, ngenxa yam nangenxa yeendaba ezilungileyo, wowusindisa.
|
1.242279 |
Mwamuna amene akufuna kukwatira ayenera kukonzekera udindo wake.
|
Indoda efuna ukutshata ifanele iyilungele le mbopheleleko.
|
1.242277 |
Pakuti kumene kuli awiri kapena atatu asonkhanira m'dzina langa, ndiri komweko pakati pao.
|
Kuba apho bahlanganisene khona egameni lam, nokuba babini nokuba bathathu, ndikho mna apho phakathi kwabo.
|
1.242273 |
Choncho kulimbikitsana wina ndi mzake ndi mawu awa.
|
Ngoko ke thuthuzelanani ngala mazwi.
|
1.242269 |
Melbourne, palibe amene amagona usiku uliwonse!
|
Melbourne, akukho mntu ulala ubusuku ngabunye!
|
1.242269 |
Pali kwalembedwa, kuti Abrahmu adali nawo ana amuna awiri, mmodzi mwa mdzakazi, ndi m'modzi mwa mkazi waufulu.
|
Kuba kubhaliwe kwathiwa, uAbraham wayenoonyana ababini: omnye engowekhobokazana, omnye engowomfazi okhululekileyo.
|
1.242217 |
Pakuti iye adzakhala wamkulu pamaso pa Ambuye, ndipo sadzamwa konse vinyo kapena kachasu; nadzadzazidwa ndi Mzimu Woyera, kuyambira asanabadwe.
|
Yena uya kubaluleka eNkosini, angaseli wayini nasiselo sinxilisayo, alawulwe nguMoya oyiNgcwele kwasekuzalweni kwakhe.
|
1.242216 |
2:12 Ichi chidzakhala chizindikiro kwa inu: mudzapeza mwana wakhanda wokutidwa ndi nsalu atagona modyera. "
|
2:12 Kwaye oku kuya kuba ngumqondiso kuwe: uya kufumana usana lusongelwe eziqhiyeni, lulele emkhumbini wesitali. "
|
1.242197 |
pakuti chipatso cha kuunika tichipeza m'ubwino wonse, ndi chilungamo, ndi choonadi,
|
Kuba sona isiqhamo soMoya sikuko konke ukulunga, nobulungisa, nenyaniso;
|
1.242196 |
Poti ndiwe mwana, nthawi zina mwina ungachite mantha kutsatira malamulo a Mulungu.
|
Njengomntu oselula, maxa wambi usenokoyika ukuthobela imiyalelo kaThixo.
|
1.24216 |
6 Sindidzaopa anthu masauzande makumimakumi
|
6 Andiyi kuwoyika amashumi amawaka abantu
|
1.242158 |
'Mverani Ndipo Mumvetse Tanthauzo Lake'
|
'Phulaphulani Nize Nifumane Intsingiselo'
|
1.242156 |
Iwo sanafooke ndipo ankachita zinthu mogwirizana ndi mapemphero awo.
|
Baqhubeka besenza umzamo kwaye besenza ngokuvumelana nemithandazo yabo.
|
1.242155 |
Mwana: Masiku ano sindikufunanso zopita kumisonkhano.
|
Unyana: Mna andisakufuni ukuya ezintlanganisweni.
|
1.242154 |
nsautso ndi kuwawa mtima, kwa moyo wa munthu ali yense wakucita zoipa, kuyambira Myuda, komanso Mhelene;
|
Kuya kubakho imbandezelo nobunzima kubantu bonke abenza okubi, kumJuda kuqala kwanakowolunye uhlanga ngokunjalo.
|
1.242128 |
Pakuti amene Mulungu anawadziwiratu, anawasankhiratunso kuti akonzedwe mʼchifanizo cha Mwana wake, kuti Iye akhale Mwana woyamba kubadwa mwa abale ambiri.
|
Kaloku abo wayeselebazi kwangaphambili, wabamisela ukuba babe ngumfanekiso woNyana wakhe, ukuze uNyana wakhe abe ngowamazibulo kusapho olukhulu.
|
1.242108 |
Musalole kuti munthu akuposeni mphamvu."
|
Musa ukuvumela umntu ofayo abe namandla nxamnye nawe."
|
1.242031 |
M'mawu anuanu, fotokozani zimene zikuchitika pa chithunzi chilichonse.
|
Ngamazwi akho, chaza oko kwenzekayo kumfanekiso ngamnye.
|
1.242021 |
Iye anati: "Chifukwa chake dikirani; chifukwa simudziwa tsiku limene Ambuye wanu adzabwera ...
|
"Phaphani ngoko, kuba ningàwazi umhla wokufika kweNkosi yenu.
|
1.241993 |
Anthu Ofunika Kwambiri Kuwaphunzitsa Baibulo
|
Ezona Zifundo Zakho ZeBhayibhile Zibalulekileyo
|
1.241962 |
Kodi inunso munayamba mwamva ngati mmene Yosefe ankamveramu?
|
Ngaba wakhe wavakalelwa njengoYosefu?
|
1.24196 |
2 Nawonso angelo ndi alaliki.
|
2 Iingelosi nazo zingabavangeli.
|
1.241956 |
Malangizo: Chitani zotsatirazi muli pamalo opanda phokoso.
|
Imiyalelo: Funda ezi ndinyana zingezantsi kwindawo engenaziphazamiso.
|
1.241939 |
Yesu anawawuza kuti, "Atate anga amagwira ntchito nthawi zonse mpaka lero lino, ndipo Inenso ndili pa ntchito."
|
Wawaphendula ke uYesu wathi, UBawo uyasebenza kude kube ngoku;ndiyasebenza. "
|
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.